Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 23:3 - Buku Lopatulika

Ndipo Abrahamu anauka pa wakufa wake, nanena kwa ana a Hiti, nati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Abrahamu anauka pa wakufa wake, nanena kwa ana a Hiti, nati,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kenaka adasiya mtembo wa mkazi wakewo, nakalankhula ndi anthu a ku Hiti kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka Abrahamu ananyamuka pamene panali mtembo wa mkazi wakepo kupita kukayankhula ndi anthu a ku Hiti. Ndipo anati,

Onani mutuwo



Genesis 23:3
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Kanani anabala Sidoni woyamba wake, ndi Heti,


ndi Ahiti, ndi Aperizi, ndi Arefaimu,


Ndipo ana a Hiti anayankha Abrahamu nati kwa iye,


Ndipo anauka Abrahamu naweramira anthu a m'dzikomo, ana a Hiti.


munda umene anagula Abrahamu kwa ana a Hiti. Pamenepo anamuika Abrahamu ndi Sara mkazi wake.


Ndipo anati Rebeka kwa Isaki, Ndalema moyo wanga chifukwa cha ana aakazi a Ahiti, akatenga Yakobo mkazi wa ana aakazi a Ahiti, onga ana aakazi a m'dziko lino, moyo wanga udzandikhalira ine bwanji?


m'phanga lili m'munda wa Makipela, umene uli patsogolo pa Mamure, m'dziko la Kanani, limene Abrahamu analigula kwa Efuroni Muhiti pamodzi ndi munda, likhale poikira pake:


Uriya Muhiti; onse pamodzi anali makumi atatu mphambu asanu ndi awiri.


Pamenepo Davide anayankha nati kwa Ahimeleki Muhiti, ndi Abisai, mwana wa Zeruya, mbale wake wa Yowabu, nati, Adzatsikira nane ndani kumisasako kwa Saulo? Nati Abisai, Nditsika nanu ndine.