Genesis 25:10 - Buku Lopatulika10 munda umene anagula Abrahamu kwa ana a Hiti. Pamenepo anamuika Abrahamu ndi Sara mkazi wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 munda umene anagula Abrahamu kwa ana a Hiti: pamenepo anamuika Abrahamu ndi Sara mkazi wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Unali munda umene Abrahamu adaagula kwa Ahiti. Abrahamu ndi mkazi wake Sara adaikidwa kumeneko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 uwu ndi munda umene Abrahamu anagula kwa Ahiti. Kumeneko Abrahamu anakayikidwa pamodzi ndi mkazi wake Sara. Onani mutuwo |