Genesis 25:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo panali atafa Abrahamu, Mulungu anamdalitsa Isaki mwana wake; ndipo Isaki anakhala pa Beere-Lahai-Roi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo panali atafa Abrahamu, Mulungu anamdalitsa Isaki mwana wake; ndipo Isaki anakhala pa Beere-Lahai-Roi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Atamwalira Abrahamu, Mulungu adadalitsa mwana wake Isaki amene ankakhala pafupi ndi chitsime cha Wamoyo-Wondipenya chija. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Atamwalira Abrahamu, Mulungu anadalitsa mwana wake Isake, amene ankakhala pafupi ndi Beeri-lahai-roi (chitsime cha Wamoyo Wondipenya). Onani mutuwo |