Genesis 25:12 - Buku Lopatulika12 Mibadwo ya Ismaele mwana wamwamuna wa Abrahamu, amene Hagara Mwejipito mdzakazi wa Sara anambalira Abrahamu ndi iyi: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Mibadwo ya Ismaele mwana wamwamuna wake wa Abrahamu, amene Hagara Mwejipito mdzakazi wa Sara anambalira Abrahamu ndi iyi: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Nazi zidzukulu za Ismaele, mwana wa Abrahamu amene adamubalira Hagara, mdzakazi wa ku Ejipito uja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Nazi zidzukulu za Ismaeli, mwana wa Abrahamu amene wantchito wa Sara, Hagara Mwigupto uja, anaberekera Abrahamu. Onani mutuwo |