Genesis 25:13 - Buku Lopatulika13 ndipo maina a ana a Ismaele, maina ao m'mibadwo yao ndi awa: woyamba wa Ismaele ndi Nebayoti; ndi Kedara, ndi Adibeele, ndi Mibisamu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 ndipo maina a ana a Ismaele, maina ao m'mibadwo yao ndi awa: woyamba wa Ismaele ndi Nebayoti; ndi Kedara, ndi Adibeele, ndi Mibisamu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Maina a ana a Ismaele ndi aŵa: woyamba anali Nebayoti, pambuyo pake adabereka Kedara, Adibeele, Mibisamu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Awa ndi mayina a ana a Ismaeli monga mwa mndandanda wa mabadwidwe awo: Nebayoti ndiye anali mwana woyamba wa Ismaeli; kenaka Kedara, Adibeeli, Mibisamu, Onani mutuwo |