Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 15:20 - Buku Lopatulika

20 ndi Ahiti, ndi Aperizi, ndi Arefaimu,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 ndi Ahiti, ndi Aperizi, ndi Arefaimu,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 la Ahiti, la Aperizi, la Arefaimu,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Ahiti, Aperezi, Arefaimu,

Onani mutuwo Koperani




Genesis 15:20
9 Mawu Ofanana  

Ndipo panali ndeu, abusa a Abramu kudana ndi abusa a Loti. Akanani ndi Aperizi ndipo analinkukhala nthawi yomweyo m'dzikomo.


Chaka chakhumi ndi chinai ndipo anadza Kedorilaomere ndi mafumu amene anali naye, nawakantha Arefaimu mu Asiteroti-Karanaimu, ndi Azuzimu mu Hamu, ndi Aemimu mu Savekiriyataimu,


Akeni ndi Akenizi, Akadimoni,


ndi Aamori, ndi Akanani, ndi Agirigasi, ndi Ayebusi.


Ndipo Abrahamu anauka pa wakufa wake, nanena kwa ana a Hiti, nati,


Ndipo padzakhala ngati wamasika alikumweta tirigu wosacheka, ndi dzanja lake lilikudula ngala; inde padzakhala ngati pamene wina akunkha ngala m'chigwa cha Refaimu.


Aamaleke akhala m'dziko la kumwera; ndi Ahiti, ndi Ayebusi, ndi Aamori, akhala ku mapiri, ndi Akanani akhala kunyanja, ndi m'mphepete mwa Yordani.


koma muwaononge konse Ahiti, ndi Aamori, Akanani, ndi Aperizi, Ahivi ndi Ayebusi; monga Yehova Mulungu wanu anakulamulirani;


Ndipo Yoswa ananena nao, Ngati muli anthu aunyinji, kwerani kuli mitengoko, ndi kudziswera minda m'dziko la Aperizi ndi la Arefaimu; akakucheperani malo kuphiri la Efuremu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa