Genesis 23:4 - Buku Lopatulika4 Ine ndine mlendo wakukhala ndi inu: mundipatse ndikhale ndi manda pamodzi ndi inu, kuti ndiike wakufa wanga ndisamthirenso maso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ine ndine mlendo wakukhala ndi inu: mundipatse ndikhale ndi manda pamodzi ndi inu, kuti ndiike wakufa wanga ndisamthirenso maso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 “Ine ndine mlendo kwanu kuno, wongoyenda. Mundigulitseko kadziko kuti kakhale manda, kuti ndiike mkazi wanga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 “Ine ndine mlendo wongoyendayenda kwanu kuno. Bwanji mundigulitse malo woti akhale manda kuti ndiyikepo thupi la mkazi wanga.” Onani mutuwo |