Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 23:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo ana a Hiti anayankha Abrahamu nati kwa iye,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo ana a Hiti anayankha Abrahamu nati kwa iye,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Anthuwo adamuyankha kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Anthu a ku Hiti aja anamuyankha Abrahamu kuti,

Onani mutuwo Koperani




Genesis 23:5
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Kanani anabala Sidoni woyamba wake, ndi Heti,


Ndipo Abrahamu anauka pa wakufa wake, nanena kwa ana a Hiti, nati,


Ine ndine mlendo wakukhala ndi inu: mundipatse ndikhale ndi manda pamodzi ndi inu, kuti ndiike wakufa wanga ndisamthirenso maso.


Mutimvere ife mfumu, ndinu kalonga wamkulu pakati pa ife; muike wakufa wanu m'manda mwathu mosankhika: palibe munthu yense wa ife adzakaniza manda ake, kuti muike wakufa wanu.


Ndi Kanani anabala Sidoni mwana wake woyamba, ndi Heti,


Koma aika waumphawi pamsanje posazunzika, nampatsa mabanja ngati gulu la nkhosa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa