Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 2:11 - Buku Lopatulika

Dzina la woyamba ndi Pisoni: umenewo ndiwo wozungulira dziko lonse la Havila, m'mene muli golide;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Dzina la wakuyamba Pisoni: umenewo ndiwo wozungulira dziko lonse la Havila, m'mene muli golide;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mtsinje woyamba ndi Pisoni, ndipo umayenda mozungulira dziko la Havila, kumene kumapezeka golide.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Dzina la mtsinje woyamba ndi Pisoni; uwu umazungulira dziko lonse la Havila, kumene kuli golide.

Onani mutuwo



Genesis 2:11
9 Mawu Ofanana  

ndi Ofiri ndi Havila, ndi Yobabu; onse amenewa ndi ana a Yokotani.


Ndi ana aamuna a Kusi: Seba, ndi Havila, ndi Sabita, ndi Raama, ndi Sabiteka; ndi ana a Raama: Sheba ndi Dedani.


golide wa dziko ali wabwino; ndimonso muli bedola ndi mwala wasohamu.


Dzina la mtsinje wachiwiri ndi Gihoni: umenewo ndiwo wozungulira dziko lonse la Kusi.


Ndipo anakhala iwo kuyambira ku Havila kufikira ku Suri, ndiko kum'mawa kwake kwa Ejipito, pakunka ku Asiriya: ndipo iye anakhala pamaso pa abale ake onse.


ndi Ofiri, ndi Havila, ndi Yobabu. Awa onse ndiwo ana a Yokotani.


Koma kuli mtapo wa siliva, ndi malo a golide amene amuyenga.


Efuremu andizinga ndi bodza, ndi nyumba ya Israele ndi chinyengo, ndi Yuda apikisana ndi Mulungu, ndiye Woyera wokhulupirika.


Ndipo Saulo anakantha Aamaleke, kuyambira pa Havila, dera la ku Suri, chili pandunji pa Ejipito.