Hoseya 11:12 - Buku Lopatulika12 Efuremu andizinga ndi bodza, ndi nyumba ya Israele ndi chinyengo, ndi Yuda apikisana ndi Mulungu, ndiye Woyera wokhulupirika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Efuremu andizinga ndi bodza, ndi nyumba ya Israele ndi chinyengo, ndi Yuda apikisana ndi Mulungu, ndiye Woyera wokhulupirika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Chauta akuti, “Anthu a ku Efuremu andizinga ndi mabodza. Banja limeneli la Israele nlonama kwambiri. Nawonso anthu a ku Yuda akundipandukirabe Ine Mulungu, Woyera ndi wokhulupirika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Efereimu wandizungulira ndi mabodza, nyumba ya Israeli yandizungulira ndi chinyengo. Ndipo Yuda wawukira Mulungu, wawukira ngakhale Woyerayo amene ndi wokhulupirika. Onani mutuwo |