Hoseya 12:1 - Buku Lopatulika1 Efuremu akudya mphepo, natsata mphepo ya kum'mawa; tsiku lonse achulukitsa mabodza ndi chipasuko, ndipo achita pangano ndi Asiriya, natenga mafuta kunka nao ku Ejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Efuremu akudya mphepo, natsata mphepo ya kum'mawa; tsiku lonse achulukitsa mabodza ndi chipasuko, ndipo achita pangano ndi Asiriya, natenga mafuta kunka nao ku Ejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Efuremu chakudya chake ndi mpweya wokhawokha. Amanka nasaka mphepo yakuvuma tsiku lonse. Amachulukitsa mabodza ndi chiwawa. Amachita chipangano ndi dziko la Asiriya, ndipo amapereka mitulo ya mafuta ku Ejipito.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Efereimu amadya mpweya; tsiku lonse amasaka mphepo ya kummawa ndipo amachulukitsa mabodza ndi chiwawa. Amachita mgwirizano ndi Asiriya ndipo amatumiza mphatso za mafuta a olivi ku Igupto. Onani mutuwo |