Hoseya 12:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Yehova ali ndi mlandu ndi Yuda, nadzalanga Yakobo monga mwa njira zake, adzambwezera monga mwa machitidwe ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Yehova ali ndi mlandu ndi Yuda, nadzalanga Yakobo monga mwa njira zake, adzambwezera monga mwa machitidwe ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Chauta akuŵaimba mlandu anthu a ku Yuda. Adzalanga a m'banja la Yakobe chifukwa cha makhalidwe ao, adzaŵabwezera zolingana ndi ntchito zao zoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Yehova akuyimba mlandu Yuda; Iye adzalanga Yakobo molingana ndi makhalidwe ake, adzamulanga molingana ndi ntchito zake. Onani mutuwo |