Hoseya 11:11 - Buku Lopatulika11 Adzafika ndi kunjenjemera ngati mbalame ya ku Ejipito, ndi ngati nkhunda m'dziko la Asiriya; ndipo ndidzawakhalitsa m'nyumba zao, ati Yehova Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Adzafika ndi kunjenjemera ngati mbalame ya ku Ejipito, ndi ngati nkhunda m'dziko la Asiriya; ndipo ndidzawakhalitsa m'nyumba zao, ati Yehova Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Adzabwera akunjenjemera ngati mbalame kuchokera ku Ejipito, adzabwera ngati njiŵa kuchokera ku Asiriya. Motero ndidzaŵabwezeranso kwao. Ndikutero Ine Chauta.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Adzabwera akunjenjemera ngati mbalame kuchokera ku Igupto, ngati nkhunda kuchokera ku Asiriya. Ine ndidzawakhazikanso mʼnyumba zawo,” akutero Yehova. Onani mutuwo |