Genesis 2:12 - Buku Lopatulika12 golide wa dziko ali wabwino; ndimonso muli bedola ndi mwala wasohamu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 golide wa dziko ali wabwino; ndimonso muli bedola ndi mwala wasohamu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 (Golide wakumeneko ndi wabwino. Kumapezekanso bedeliyo ndi miyala ya mtengowapatali yotchedwa onikisi.) Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 (Golide wa ku dziko ili ndi wabwino. Kulinso miyala yokongola ya bedola ndi onikisi). Onani mutuwo |