Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 2:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 (Golide wa ku dziko ili ndi wabwino. Kulinso miyala yokongola ya bedola ndi onikisi).

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

12 golide wa dziko ali wabwino; ndimonso muli bedola ndi mwala wasohamu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 golide wa dziko ali wabwino; ndimonso muli bedola ndi mwala wasohamu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 (Golide wakumeneko ndi wabwino. Kumapezekanso bedeliyo ndi miyala ya mtengowapatali yotchedwa onikisi.)

Onani mutuwo Koperani




Genesis 2:12
8 Mawu Ofanana  

Dzina la mtsinje woyamba ndi Pisoni; uwu umazungulira dziko lonse la Havila, kumene kuli golide.


Dzina la mtsinje wachiwiri ndi Gihoni; uwu umazungulira dziko lonse la Kusi.


Nzeru singagulidwe ndi golide wa ku Ofiri, kapena ndi miyala ya onikisi kapena ya safiro.


miyala yokongola ya mtundu wa onikisi ndi ina yabwino yoyika pa efodi ndi pa chovala cha pachifuwa.


Mzere wachinayi pakhale miyala ya topazi, onikisi ndi yasipa. Miyalayi uyiike mu zoyikamo zagolide.


mzere wachinayi anayikapo miyala ya topazi, onikisi ndi yasipa. Miyalayi anayiyika mu zoyikamo zagolide.


Iwe unkakhala ngati mu Edeni, munda wa Mulungu. Miyala yokongola ya mitundu yonse: rubi, topazi ndi dayimondi, kirisoliti, onikisi, yasipa, safiro, kalineliyoni ndi berili ndiwo inali zofunda zako. Ndipo zoyikamo miyalayo zinali zagolide. Anakupangira zonsezi pa tsiku limene unalengedwa.


Mana ankafanana ndi mbewu zamapira ndipo maonekedwe ake anali ngati ulimbo wowuma.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa