1 Samueli 15:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo Saulo anakantha Aamaleke, kuyambira pa Havila, dera la ku Suri, chili pandunji pa Ejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo Saulo anakantha Aamaleke, kuyambira pa Havila, dera la ku Suri, chili pandunji pa Ejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Pamenepo Saulo adagonjetsa Aamaleke kuyambira ku Havila mpaka ku Suri, kuvuma kwa Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Tsono Sauli anakantha Aamaleki kuchokera ku Havila mpaka ku Suri, kummawa kwa Igupto. Onani mutuwo |