Genesis 10:7 - Buku Lopatulika7 Ndi ana aamuna a Kusi: Seba, ndi Havila, ndi Sabita, ndi Raama, ndi Sabiteka; ndi ana a Raama: Sheba ndi Dedani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndi ana amuna a Kusi: Seba, ndi Havila, ndi Sabita, ndi Raama, ndi Sabiteka; ndi ana a Raama: Sheba ndi Dedani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ana a Kusi anali Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka. Ana a Raama anali Sheba ndi Dedani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ana aamuna a Kusi anali: Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka. Ana aamuna a Raama anali: Seba ndi Dedani. Onani mutuwo |