Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 10:6 - Buku Lopatulika

6 Ndi ana aamuna a Hamu: Kusi, ndi Ejipito, ndi Puti, ndi Kanani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndi ana amuna a Hamu: Kusi, ndi Ejipito, ndi Puti, ndi Kanani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Ana a Hamu anali Kusi, Ejipito, Libia ndi Kanani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 10:6
15 Mawu Ofanana  

Amenewo ndipo anagawa zisumbu za amitundu m'maiko mwao, onse amene monga mwa chinenedwe chao; ndi mwa mabanja ao, ndi m'mitundu yao.


Dzina la mtsinje wachiwiri ndi Gihoni: umenewo ndiwo wozungulira dziko lonse la Kusi.


Ndipo Nowa anali wa zaka mazana asanu; ndipo Nowa anabala Semu ndi Hamu ndi Yafeti.


Ndi ana aamuna a Nowa amene anatuluka m'chingalawa ndiwo Semu, ndi Hamu, ndi Yafeti. Hamu ndiye atate wake wa Kanani.


Ndipo Hamu atate wake wa Kanani, anauona umaliseche wa atate wake, nauza abale ake awiri amene anali kunja.


Ndipo anapeza podyetsa ponenepetsa ndi pabwino, ndipo dzikoli ndi lachitando ndi lodikha ndi losungikamo, pakuti okhalako kale ndiwo a Hamu.


Pamenepo Israele analowa mu Ejipito; ndi Yakobo anakhala mlendo m'dziko la Hamu.


Anaika pakati pao zizindikiro zake, ndi zodabwitsa m'dziko la Hamu.


zodabwitsa m'dziko la Hamu, zoopsa ku Nyanja Yofiira.


Ndipo anapha ana oyamba onse a mu Ejipito, ndiwo oyamba a mphamvu yao m'mahema a Hamu.


Ndipo padzakhala tsiku lomwelo, kuti Ambuye adzabweza kachiwiri ndi dzanja lake anthu ake otsala ochokera ku Asiriya, ndi ku Ejipito, ndi ku Patirosi, ndi ku Kusi, ndi ku Elamu, ndi ku Sinara, ndi ku Hamati, ndi ku zisumbu za m'nyanja.


Kwerani, inu akavalo; chitani misala, inu magaleta, atuluke amphamvu; Akusi ndi Aputi, ogwira chikopa; ndi Aludi, amene agwira ndi kukoka uta.


Apersiya, Aludi, Aputi, anali m'khamu lako; anthu ako a nkhondo anapachika chikopa ndi chisoti mwa iwe, anamveketsa kukoma kwako.


Persiya, Kusi, ndi Puti pamodzi nao, onsewo ndi chikopa ndi chisoti chachitsulo;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa