Genesis 10:6 - Buku Lopatulika6 Ndi ana aamuna a Hamu: Kusi, ndi Ejipito, ndi Puti, ndi Kanani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndi ana amuna a Hamu: Kusi, ndi Ejipito, ndi Puti, ndi Kanani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ana a Hamu anali Kusi, Ejipito, Libia ndi Kanani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani. Onani mutuwo |