Genesis 10:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo Kusi anabala Nimirodi; ndipo iye anayamba kukhala wamphamvu padziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo Kusi anabala Nimirodi; ndipo iye anayamba kukhala wamphamvu pa dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Kusi adabereka Nimirodi. Nimirodi anali wankhondo woyamba wanyonga pa dziko lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Kusi anabereka Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi. Onani mutuwo |