Genesis 25:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo anakhala iwo kuyambira ku Havila kufikira ku Suri, ndiko kum'mawa kwake kwa Ejipito, pakunka ku Asiriya: ndipo iye anakhala pamaso pa abale ake onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo anakhala iwo kuyambira ku Havila kufikira ku Suri, ndiko kum'mawa kwake kwa Ejipito, pakunka ku Asiriya: ndipo iye anakhala pamaso pa abale ake onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Zidzukulu za Ismaeleyo zinkakhala m'dziko la pakati pa Havila ndi Suri, kuvuma kwa Ejipito, pa njira ya ku Asiriya. Zinkakhala molekana ndi zidzukulu zina za Abrahamu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Zidzukulu za Ismaeli zinkakhala mʼdera la pakati pa Havila ndi Suri, kummwera kwa Igupto, mukamapita cha ku Asuri. Choncho anakhala kummawa kwa abale awo. Onani mutuwo |