Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Filemoni 1:11 - Buku Lopatulika

amene kale sanakupindulire, koma tsopano watipindulira bwino iwe ndi ine;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

amene kale sanakupindulira, koma tsopano watipindulira bwino iwe ndi ine;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kale unalibe naye ntchito, koma tsopano angathe kutithandiza kwambiri tonsefe, iweyo ndi ine ndemwe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anali wopanda phindu kwa iwe, koma tsopano wasanduka wa phindu kwa iwe ndi kwa inenso.

Onani mutuwo



Filemoni 1:11
10 Mawu Ofanana  

Ndipo ponyani kapoloyo wopanda pake kumdima wakunja; kumene kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.


chifukwa mwana wanga uyu anali wakufa, ndipo akhalanso wamoyo; anali wotayika, ndipo wapezedwa. Ndipo anayamba kusekera.


Koma kudayenera kuti tisangalale ndi kukondwerera: chifukwa mng'ono wako uyu anali wakufa ndipo ali ndi moyo; anatayika, ndipo wapezeka.


Chotero inunso m'mene mutachita zonse anakulamulirani, nenani, Ife ndife akapolo opanda pake, tangochita zimene tayenera kuzichita.


onsewa apatuka, pamodzi akhala opanda pake; palibe mmodzi wakuchita zabwino, inde, palibe mmodzi ndithu.


Luka yekha ali pamodzi ndi ine. Umtenge Marko, adze pamodzi ndi iwe; pakuti ayenera kunditumikira.


ndikudandaulira chifukwa cha mwana wanga, amene ndambala m'ndende, Onesimo,


amene ndi yemweyo ndakubwezera iwe, ndiye mtima weniweni wa ine.


inu amene kale simunali anthu, koma tsopano muli anthu a Mulungu; amene kale simunalandire chifundo, koma tsopano mwalandira chifundo.