Luka 15:24 - Buku Lopatulika24 chifukwa mwana wanga uyu anali wakufa, ndipo akhalanso wamoyo; anali wotayika, ndipo wapezedwa. Ndipo anayamba kusekera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 chifukwa mwana wanga uyu anali wakufa, ndipo akhalanso wamoyo; anali wotayika, ndipo wapezedwa. Ndipo anayamba kusekera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Chifukwa mwana wangayu adaafa, koma tsopano wakhalanso moyo; adaatayika, koma tsopano wapezeka.’ Ndiye pompo chikondwerero chidayamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Pakuti mwana wangayu anali wakufa, ndipo ali ndi moyonso; iye anatayika ndipo wapezeka.’ Chomwecho anayamba kukondwerera. Onani mutuwo |