Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 17:10 - Buku Lopatulika

10 Chotero inunso m'mene mutachita zonse anakulamulirani, nenani, Ife ndife akapolo opanda pake, tangochita zimene tayenera kuzichita.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Chotero inunso m'mene mutachita zonse anakulamulirani, nenani, Ife ndife akapolo opanda pake, tangochita zimene tayenera kuzichita.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Choncho inunso, mutachita zonse zimene adakulamulani, muziti, ‘Ndife antchito osayenera kulandira kanthu. Tangochita zimene tinayenera kuchita.’ ”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Chimodzimodzi inunso, mukachita zonse zimene munawuzidwa, muzinena kuti, ‘Ndife antchito osayenera; tangogwira ntchito yathu basi.’ ”

Onani mutuwo Koperani




Luka 17:10
20 Mawu Ofanana  

Ndipo ine ndinati, Tsoka kwa ine! Chifukwa ndathedwa; chifukwa ndili munthu wa milomo yonyansa, ndikhala pakati pa anthu a milomo yonyansa; chifukwa kuti maso anga aona Mfumu, Yehova wa makamu.


Pakuti ife tonse takhala ngati wina amene ali wosakonzeka; ndi zolungama zathu zonse zili ngati chovala chodetsedwa; ndipo ife tonse tifota monga tsamba, ndi zoipa zathu zitiuluza monga mphepo.


ndipo analowa, nakhalamo; koma sanamvere mau anu, sanayende m'chilamulo chanu; sanachite kanthu ka zonse zimene munawauza achite; chifukwa chake mwafikitsa pa iwo choipa chonsechi;


Ndipo ponyani kapoloyo wopanda pake kumdima wakunja; kumene kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.


Ndipo kunali, pakumuka ku Yerusalemu Iye analikupita pakati pa Samariya ndi Galileya.


Kodi ayamika kapoloyo chifukwa anachita zolamulidwa?


Ndipo anayamba ndani kumpatsa Iye, ndipo adzambwezeranso?


onsewa apatuka, pamodzi akhala opanda pake; palibe mmodzi wakuchita zabwino, inde, palibe mmodzi ndithu.


amene kale sanakupindulire, koma tsopano watipindulira bwino iwe ndi ine;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa