Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 17:9 - Buku Lopatulika

9 Kodi ayamika kapoloyo chifukwa anachita zolamulidwa?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Kodi ayamika kapoloyo chifukwa anachita zolamulidwa?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Kodi ungamthokoze wantchitoyo chifukwa chakuti wachita zimene unamlamula?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Kodi iye angathokoze wantchitoyo chifukwa chochita chimene anawuzidwa kuchita?

Onani mutuwo Koperani




Luka 17:9
2 Mawu Ofanana  

Chotero inunso m'mene mutachita zonse anakulamulirani, nenani, Ife ndife akapolo opanda pake, tangochita zimene tayenera kuzichita.


wosanena naye makamaka, Undikonzere chakudya ine, nudzimangire, nunditumikire kufikira ndadya ndi kumwa; ndipo nditatha ine udzadya nudzamwa iwe?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa