Filemoni 1:11 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Anali wopanda phindu kwa iwe, koma tsopano wasanduka wa phindu kwa iwe ndi kwa inenso. Onani mutuwoBuku Lopatulika11 amene kale sanakupindulire, koma tsopano watipindulira bwino iwe ndi ine; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 amene kale sanakupindulira, koma tsopano watipindulira bwino iwe ndi ine; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Kale unalibe naye ntchito, koma tsopano angathe kutithandiza kwambiri tonsefe, iweyo ndi ine ndemwe. Onani mutuwo |