Mateyu 25:30 - Buku Lopatulika30 Ndipo ponyani kapoloyo wopanda pake kumdima wakunja; kumene kudzakhala kulira ndi kukukuta mano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndipo ponyani kapoloyo wopanda pake kumdima wakunja; kumene kudzakhala kulira ndi kukukuta mano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Tsono mtumiki wopandapakeyu kamponyeni kunja ku mdima. Kumeneko azikalira ndi kukukuta mano.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Ndipo muponyeni wantchito wopanda phinduyu kunja, ku mdima kumene kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.’ ” Onani mutuwo |