Filemoni 1:10 - Buku Lopatulika10 ndikudandaulira chifukwa cha mwana wanga, amene ndambala m'ndende, Onesimo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 ndikudandaulira chifukwa cha mwana wanga, amene ndambala m'ndende, Onesimo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndikukupempha chifukwa cha mwana wanga mwa Khristu, amene ndidachita ngati kumubala m'ndende muno. Iyeyu ndi Onesimo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 ndikukupempha chifukwa cha mwana wanga Onesimo, amene ndamubala ndili mu unyolo. Onani mutuwo |