Filemoni 1:9 - Buku Lopatulika9 koma makamaka ndidandaulira mwa chikondi, pokhala wotere, Paulo nkhalamba, ndipo tsopano wandendenso wa Khristu Yesu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 koma makamaka ndidandaulira mwa chikondi, pokhala wotere, Paulo nkhalamba, ndipo tsopano wandendenso wa Khristu Yesu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Komabe chifukwa cha chikondi makamaka ndingochita kukupempha, ine Paulo amene ndili nkhalamba, amenenso ndili m'ndende tsopano chifukwa cha Khristu Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 komabe ndikupempha mwachikondi. Ine Paulo, munthu wokalamba, ndipo tsopano ndili mʼndende chifukwa cha Khristu Yesu, Onani mutuwo |