Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Timoteyo 4:11 - Buku Lopatulika

11 Luka yekha ali pamodzi ndi ine. Umtenge Marko, adze pamodzi ndi iwe; pakuti ayenera kunditumikira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Luka yekha ali pamodzi ndi ine. Umtenge Marko, adze pamodzi ndi iwe; pakuti ayenera kunditumikira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Luka yekha ndiye ali ndi ine. Ukatenge Marko udzabwere naye kuno, chifukwa amene uja angathe kundithandiza pa ntchito.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Ndatsala ndi Luka yekha basi. Mutenge Marko ndipo ubwere naye kuno, chifukwa amandithandiza mu utumiki wanga.

Onani mutuwo Koperani




2 Timoteyo 4:11
15 Mawu Ofanana  

Ndidzachiritsa kubwerera kwao, ndidzawakonda mwaufulu; pakuti mkwiyo wanga wamchokera.


Koma ambiri oyamba adzakhala akuthungo, ndi akuthungo adzakhala oyamba.


Chomwecho omalizira adzakhala oyamba, ndipo oyamba adzakhala omalizira.


Ndipo onani, alipo akuthungo amene adzakhala oyamba, ndipo alipo oyamba adzakhala akuthungo.


Ndipo m'mene adalingirirapo, anadza kunyumba ya Maria amake wa Yohane wonenedwanso Marko; pamenepo ambiri adasonkhana pamodzi, ndipo analikupemphera.


Ndipo Barnabasi ndi Saulo anabwera kuchokera ku Yerusalemu m'mene adatsiriza utumiki wao, natenga Yohane wonenedwanso Marko amuke nao.


Ndipo Barnabasi anafuna kumtenga Yohane uja, wotchedwa Marko


Ndipo panali kupsetsana mtima, kotero kuti analekana wina ndi mnzake; ndipo Barnabasi anatenga Marko, nalowa m'ngalawa, nanka ku Kipro.


Pamene anaona masomphenyawo, pomwepo tinayesa kutulukira kunka ku Masedoniya, poganizira kuti Mulungu anaitanira ife kulalikira Uthenga Wabwino kwa iwo.


Aristariko wam'ndende mnzanga akupatsani moni, ndi Marko, msuweni wa Barnabasi (amene munalandira zolamulira za kwa iye; akafika kwanu, mumlandire iye),


Akupatsani moni Luka sing'anga wokondedwa, ndi Dema.


Ichi uchidziwa, kuti onse a mu Asiya adabwerera kusiyana nane; a iwo ali Figelo ndi Heremogene.


Ngati tsono munthu adziyeretsa yekha pa izi, adzakhala chotengera cha kuulemu, chopatulidwa, choyenera kuchita nacho Mbuye, chokonzera ntchito yonse yabwino.


ateronso, Marko, Aristariko, Dema, Luka, antchito anzanga.


Iye wa ku Babiloni wosankhidwa pamodzi nanu akukupatsani moni; ateronso Marko mwana wanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa