2 Timoteyo 4:11 - Buku Lopatulika11 Luka yekha ali pamodzi ndi ine. Umtenge Marko, adze pamodzi ndi iwe; pakuti ayenera kunditumikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Luka yekha ali pamodzi ndi ine. Umtenge Marko, adze pamodzi ndi iwe; pakuti ayenera kunditumikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Luka yekha ndiye ali ndi ine. Ukatenge Marko udzabwere naye kuno, chifukwa amene uja angathe kundithandiza pa ntchito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ndatsala ndi Luka yekha basi. Mutenge Marko ndipo ubwere naye kuno, chifukwa amandithandiza mu utumiki wanga. Onani mutuwo |