Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 2:4 - Buku Lopatulika

Mauta a amphamvu anathyoka, koma okhumudwawo amangiridwa ndi mphamvu m'chuuno.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mauta a amphamvu anathyoka, koma okhumudwawo amangiridwa ndi mphamvu m'chuuno.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ankhondo amphamvu mauta ao athyoka, koma anthu ofooka avala dzilimbe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Mauta a anthu ankhondo athyoka koma anthu ofowoka avala dzilimbe.

Onani mutuwo



1 Samueli 2:4
16 Mawu Ofanana  

Pakuti mwandizingiza mphamvu m'chuuno ku nkhondoyo; mwandigonjetsera amene andiukira.


Lupanga lao lidzalowa m'mtima mwao momwe, ndipo mauta ao adzathyoledwa.


Pakuti manja a oipa adzathyoledwa, koma Yehova achirikiza olungama.


Khalani chete, ndipo dziwani kuti Ine ndine Mulungu, Ndidzabuka mwa amitundu, ndidzabuka padziko lapansi.


Aletsa nkhondo ku malekezero a dziko lapansi; athyola uta, nadula nthungo; atentha magaleta ndi moto.


Pomwepo anathyola mivi ya pauta; chikopa, ndi lupanga, ndi nkhondo.


Adzangoweramira pansi pa andende, ndipo adzagwa pansi pa ophedwa. Mwa izi zonse mkwiyo wake sunachoke, koma dzanja lake lili chitambasulire.


Iye alimbitsa olefuka, naonjezera mphamvu iye ameme alibe mphamvu.


Pakuti ngakhale mukadakantha nkhondo yonse ya Ababiloni akumenyana nanu, ngakhale akadatsala olasidwa okhaokha mwa iwo, koma iwowa akadauka yense m'hema wake ndi kutentha mzinda uwu ndi moto.


pakuti wakufunkha wafika kwa iye, kwa Babiloni, ndi anthu ake olimba agwidwa, mauta ao athyokathyoka, pakuti Yehova ndiye Mulungu wakubwezera, adzabwezera ndithu.


Ndipo ananena kwa ine, Chisomo changa chikukwanira; pakuti mphamvu yanga ithedwa mu ufooko. Chifukwa chake makamaka ndidzadzitamandira mokondweratu m'mafooko anga, kuti mphamvu ya Khristu ikhale pa ine.


Chifukwa chake chilimikani, mutadzimangira m'chuuno mwanu ndi choonadi, mutavalanso chapachifuwa cha chilungamo;


Ndikhoza zonse mwa Iye wondipatsa mphamvuyo.


Ndipo ndinene chiyaninso? Pakuti idzandiperewera nthawi ndifotokozere za Gideoni, Baraki, Samisoni, Yefita; za Davide, ndi Samuele ndi aneneri;


nazima mphamvu ya moto, napulumuka lupanga lakuthwa, analimbikitsidwa pokhala ofooka, anakula mphamvu kunkhondo, anapirikitsa magulu a nkhondo yachilendo.