Aefeso 6:14 - Buku Lopatulika14 Chifukwa chake chilimikani, mutadzimangira m'chuuno mwanu ndi choonadi, mutavalanso chapachifuwa cha chilungamo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Chifukwa chake chilimikani, mutadzimangira m'chuuno mwanu ndi choonadi, mutavalanso chapachifuwa cha chilungamo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Imirirani tsono mutavala choona ngati lamba m'chiwuno mwanu. Valani chilungamo ngati chovala chachitsulo chotchinjirizira pachifuwa panu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Tsono imani mwamphamvu, mutamangira choonadi ngati lamba mʼchiwuno mwanu, mutavala chilungamo ngati chitsulo chotchinjiriza pa chifuwa. Onani mutuwo |