Masalimo 18:39 - Buku Lopatulika39 Pakuti mwandizingiza mphamvu m'chuuno ku nkhondoyo; mwandigonjetsera amene andiukira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Pakuti mwandizingiza mphamvu m'chuuno ku nkhondoyo; mwandigonjetsera amene andiukira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Paja ndinu mudandipatsa mphamvu zomenyera nkhondo, ndinu mudandigonjetsera anthu ondiwukira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Inu munandiveka ndi mphamvu yokachitira nkhondo, munachititsa kuti ndigonjetse adani anga. Onani mutuwo |