Masalimo 76:3 - Buku Lopatulika3 Pomwepo anathyola mivi ya pauta; chikopa, ndi lupanga, ndi nkhondo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pomwepo anathyola mivi ya pauta; chikopa, ndi lupanga, ndi nkhondo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Kumeneko adathyola mivi youluzika, zishango, malupanga ndi zida zonse zankhondo za adani ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kumeneko Iye anathyola mivi yowuluka, zishango ndi malupanga, zida zankhondo. Sela Onani mutuwo |