Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 76:4 - Buku Lopatulika

4 Inu ndinu wakuunikira, ndi womveka wakuposa mapiri muli achifwamba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Inu ndinu wakuunikira, ndi womveka wakuposa mapiri muli achifwamba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Inu Mulungu, mukuwonetsa ulemerero ndi mphamvu kupambana mapiri a zofunkha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Wolemekezeka ndinu, wamphamvu kuposa mapiri amene ali ndi nyama zambiri.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 76:4
8 Mawu Ofanana  

Lupanga lao lidzalowa m'mtima mwao momwe, ndipo mauta ao adzathyoledwa.


Mkango wakwera kutuluka m'nkhalango mwake, ndipo waononga amitundu ali panjira, watuluka m'mbuto mwake kuti achititse dziko lako bwinja, kuti mizinda yako ipasuke mulibenso wokhalamo.


Ndipo unayendayenda pakati pa mikango, nukhala msona, nuphunzira kugwira nyama, nulusira anthu.


ndipo ndidzakantha uta wako kuuchotsa m'dzanja lako lamanzere, ndi kutayitsa mivi yako kudzanja lako lamanja.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa