1 Samueli 2:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 “Mauta a anthu ankhondo athyoka koma anthu ofowoka avala dzilimbe. Onani mutuwoBuku Lopatulika4 Mauta a amphamvu anathyoka, koma okhumudwawo amangiridwa ndi mphamvu m'chuuno. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mauta a amphamvu anathyoka, koma okhumudwawo amangiridwa ndi mphamvu m'chuuno. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ankhondo amphamvu mauta ao athyoka, koma anthu ofooka avala dzilimbe. Onani mutuwo |