Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 3:18 - Buku Lopatulika

Ndi ana a Geresoni maina ao ndi awa, monga mwa mabanja ao: Libini, ndi Simei.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi ana a Geresoni maina ao ndi awa, monga mwa mabanja ao: Libini, ndi Simei.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono ana a Geresoni potsata mabanja ao naŵa: Labini ndi Simei.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mayina a ana a Geresoni potsata mabanja awo ndi awa: Libini ndi Simei.

Onani mutuwo



Numeri 3:18
12 Mawu Ofanana  

A Hemani, ana a Hemani: Bukiya, Mataniya, Uziyele, Sebuele, ndi Yerimoti, Hananiya, Hanani, Eliyata, Gidaliti, ndi Romamiti-Ezere, Yosibekasa, Maloti, Hotiri, Mahaziyoti;


Ndipo maina a ana a Geresomo ndi awa: Libini, ndi Simei.


Ndipo maina a ana aamuna a Levi, mwa kubadwa kwao ndiwo: Geresoni, ndi Kohati, ndi Merari; ndipo zaka za moyo wa Levi ndizo zana limodzi mphambu makumi atatu kudza zisanu ndi ziwiri.


banja la nyumba ya Levi pa lokha, ndi akazi ao pa lokha; banja la Asimei pa okha, ndi akazi ao pa okha;


Ndi ana a Kohati monga mwa mabanja ao: Amuramu ndi Izihara, Hebroni ndi Uziyele.


Banja la Libini, ndi mabanja a Simei, ndiwo a Geresoni; ndiwo mabanja a Geresoni.


Werenganso ana a Geresoni, monga mwa nyumba za makolo ao, monga mwa mabanja ao.