Zekariya 12:13 - Buku Lopatulika13 banja la nyumba ya Levi pa lokha, ndi akazi ao pa lokha; banja la Asimei pa okha, ndi akazi ao pa okha; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 banja la nyumba ya Levi pa lokha, ndi akazi ao pa lokha; banja la Asimei pa okha, ndi akazi ao pa okha; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Banja la Levi lidzalira palokha, akazi akenso adzalira paokha. Banja la Simei lidzalira palokha, akazi akenso adzalira paokha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 nyumba ya Levi pamodzi ndi akazi awo, fuko la Simei pamodzi ndi akazi awo, Onani mutuwo |