Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 1:7 - Buku Lopatulika

Wa Yuda, Nasoni mwana wa Aminadabu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wa Yuda, Nasoni mwana wa Aminadabu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

fuko la Yuda, Nasoni mwana wa Aminadabu;

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Naasoni mwana wa Aminadabu, kuchokera ku fuko la Yuda,

Onani mutuwo



Numeri 1:7
11 Mawu Ofanana  

Ndipo Aroni anadzitengera Eliseba, mwana wamkazi wa Aminadabu, mlongo wake wa Nasoni, akhale mkazi wake; ndipo anambalira Nadabu ndi Abihu, Eleazara ndi Itamara.


Wa Simeoni, Selumiele mwana wa Zurishadai.


Wa Isakara, Netanele mwana wa Zuwara.


Ndipo anayamba kuyenda ambendera ya chigono cha ana a Yuda monga mwa magulu ao; woyang'anira gulu lake ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu.


Ndipo iwo akumanga mahema ao ku m'mawa kotuluka dzuwa ndiwo a mbendera ya chigono cha Yuda, monga mwa makamu ao; ndipo kalonga wa ana Yuda ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu.


Wakubwera nacho chopereka chake tsiku loyamba ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu, wa fuko la Yuda:


mwana wa Yese, mwana wa Obede, mwana wa Bowazi, mwana wa Salimoni, mwana wa Nasoni,


Iyo ndiyo mibadwo ya Perezi; Perezi anabala Hezironi;


ndi Aminadabu anabala Nasoni, ndi Nasoni anabala Salimoni;