Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Rute 4:20 - Buku Lopatulika

20 ndi Aminadabu anabala Nasoni, ndi Nasoni anabala Salimoni;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 ndi Aminadabu anabala Nasoni, ndi Nasoni anabala Salimoni;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Aminadabu adabereka Nasoni, Nasoni adabereka Salimoni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Aminadabu abambo a Naasoni, Naasoni anali abambo a Salimoni,

Onani mutuwo Koperani




Rute 4:20
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Aroni anadzitengera Eliseba, mwana wamkazi wa Aminadabu, mlongo wake wa Nasoni, akhale mkazi wake; ndipo anambalira Nadabu ndi Abihu, Eleazara ndi Itamara.


Wa Yuda, Nasoni mwana wa Aminadabu.


Ndipo iwo akumanga mahema ao ku m'mawa kotuluka dzuwa ndiwo a mbendera ya chigono cha Yuda, monga mwa makamu ao; ndipo kalonga wa ana Yuda ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu.


ndi Ramu anabala Aminadabu; ndi Aminadabu anabala Nasoni; ndi Nasoni anabala Salimoni;


mwana wa Yese, mwana wa Obede, mwana wa Bowazi, mwana wa Salimoni, mwana wa Nasoni,


ndi Hezironi anabala Ramu, ndi Ramu anabala Aminadabu;


ndi Salimoni anabala Bowazi, ndi Bowazi anabala Obedi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa