Numeri 7:12 - Buku Lopatulika12 Wakubwera nacho chopereka chake tsiku loyamba ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu, wa fuko la Yuda: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Wakubwera nacho chopereka chake tsiku loyamba ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu, wa fuko la Yuda: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Nasoni mwana wa Aminadabu, wa fuko la Yuda, ndiye adapereka zopereka zake pa tsiku loyamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Amene anabweretsa chopereka chake tsiku loyamba anali Naasoni mwana wa Aminadabu wa fuko la Yuda. Onani mutuwo |