Numeri 7:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Amene anabweretsa chopereka chake tsiku loyamba anali Naasoni mwana wa Aminadabu wa fuko la Yuda. Onani mutuwoBuku Lopatulika12 Wakubwera nacho chopereka chake tsiku loyamba ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu, wa fuko la Yuda: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Wakubwera nacho chopereka chake tsiku loyamba ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu, wa fuko la Yuda: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Nasoni mwana wa Aminadabu, wa fuko la Yuda, ndiye adapereka zopereka zake pa tsiku loyamba. Onani mutuwo |