Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 1:6 - Buku Lopatulika

6 Wa Simeoni, Selumiele mwana wa Zurishadai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Wa Simeoni, Selumiele mwana wa Zurishadai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 fuko la Simeoni, Selumiele mwana wa Zurishadai;

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Selumieli mwana wa Zurisadai, kuchokera ku fuko la Simeoni,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 1:6
5 Mawu Ofanana  

Ndipo maina a amuna amene aime nanu ndi awa: wa Rubeni, Elizuri mwana wa Sedeuri.


Wa Yuda, Nasoni mwana wa Aminadabu.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Simeoni anayang'anira Selumiele mwana wa Zurishadai.


Ndipo iwo akumanga mahema ao poyandikizana naye ndiwo a fuko la Simeoni; ndi kalonga wa ana a Simeoni ndiye Selumiele mwana wa Zurishadai.


Tsiku lachisanu kalonga wa ana a Simeoni, ndiye Selumiele, mwana wa Zurishadai:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa