Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 1:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Selumieli mwana wa Zurisadai, kuchokera ku fuko la Simeoni,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

6 Wa Simeoni, Selumiele mwana wa Zurishadai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Wa Simeoni, Selumiele mwana wa Zurishadai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 fuko la Simeoni, Selumiele mwana wa Zurishadai;

Onani mutuwo Koperani




Numeri 1:6
5 Mawu Ofanana  

Mayina a anthu amene akuthandizeniwo ndi awa: Elizuri mwana wa Sedeuri, kuchokera ku fuko la Rubeni,


Naasoni mwana wa Aminadabu, kuchokera ku fuko la Yuda,


Mtsogoleri wa fuko la Simeoni anali Selumieli mwana wa Zurisadai,


Fuko la Simeoni lidzamanga pafupi ndi Rubeni. Mtsogoleri wa gulu la Simeoni ndi Selumieli mwana wa Zurisadai.


Pa tsiku lachisanu Selumieli mwana wa Zurisadai, mtsogoleri wa fuko la Simeoni, anabweretsa chopereka chake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa