Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 76:2 - Buku Lopatulika

Msasa wake unali mu Salemu, ndipo pokhala Iye mu Ziyoni.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Msasa wake unali m'Salemu, ndipo pokhala Iye m'Ziyoni.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Hema lake adalimanga ku Yerusalemu. Malo ake okhalamo ali kumeneko ku Ziyoni.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tenti yake ili mu Salemu, malo ake okhalamo mu Ziyoni.

Onani mutuwo



Masalimo 76:2
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Melkizedeki mfumu ya ku Salemu, anatuluka nao mkate ndi vinyo: iye ndiye wansembe wa Mulungu Wamkulukulu.


Koma ndinasankha Yerusalemu, kuti dzina langa likhale komweko; ndinasankhanso Davide akhale mfumu ya anthu anga Israele.


Chifukwa kuti pa tsiku la tsoka Iye adzandibisa mumsasa mwake, adzandibisa mkati mwa chihema chake; pathanthwe adzandikweza.


Phiri la Ziyoni, chikhalidwe chake nchokoma kumbali zake za kumpoto, ndilo chimwemwe cha dziko lonse lapansi, mzinda wa mfumu yaikulu.


Imbirani zoyamika Yehova, wokhala ku Ziyoni; lalikirani mwa anthu ntchito zake.


Tafuula, takuwa iwe, wokhala mu Ziyoni, chifukwa Woyera wa Israele wa m'kati mwako ali wamkulu.


Wachotsa mwamphamvu dindiro lake ngati la m'munda; waononga mosonkhanira mwake; Yehova waiwalitsa anthu msonkhano ndi Sabata mu Ziyoni; wanyoza mfumu ndi wansembe mokwiya mwaukali.