Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 61:3 - Buku Lopatulika

Pakuti munakhala pothawirapo panga; nsanja yolimba pothawa mdani ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti munakhala pothawirapo panga; nsanja yolimba pothawa mdani ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inutu ndinu kothaŵira kwanga, nsanja yolimba yonditeteza kwa adani.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakuti Inu mwakhala pothawirapo panga, nsanja yolimba polimbana ndi adani anga.

Onani mutuwo



Masalimo 61:3
9 Mawu Ofanana  

Popeza amanditcherera khutu lake, chifukwa chake ndidzaitanira Iye masiku anga onse.


Yehova Ambuye, ndinu mphamvu ya chipulumutso changa, munandiphimba mutu wanga tsiku lakulimbana nkhondo.


Yehova ndiye thanthwe langa, ndi linga langa, ndi Mpulumutsi wanga; Mulungu wanga, ngaka yanga, ndidzakhulupirira Iye; chikopa changa, nyanga ya chipulumutso changa, msanje wanga.


Chifukwa kuti pa tsiku la tsoka Iye adzandibisa mumsasa mwake, adzandibisa mkati mwa chihema chake; pathanthwe adzandikweza.


Pa Mulungu pali chipulumutso changa ndi ulemerero wanga. Thanthwe la mphamvu yanga ndi pothawirapo panga mpa Mulungu.


Dzina la Yehova ndilo nsanja yolimba; wolungama athamangiramo napulumuka.


amene anatilanditsa mu imfa yaikulu yotere, nadzalanditsa; amene timyembekezera kuti adzalanditsanso;