Masalimo 140:7 - Buku Lopatulika7 Yehova Ambuye, ndinu mphamvu ya chipulumutso changa, munandiphimba mutu wanga tsiku lakulimbana nkhondo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Yehova Ambuye, ndinu mphamvu ya chipulumutso changa, munandiphimba mutu wanga tsiku lakulimbana nkhondo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Inu Chauta, Ambuye anga, Mpulumutsi wanga wamphamvu, mwateteza moyo wanga pa tsiku lankhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Inu Ambuye Wamphamvuzonse, Mpulumutsi wanga wamphamvu, mumateteza mutu wanga tsiku lankhondo. Onani mutuwo |