Masalimo 140:6 - Buku Lopatulika6 Ndinati kwa Yehova, Inu ndinu Mulungu wanga; munditcherere khutu mau a kupemba kwanga, Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndinati kwa Yehova, Inu ndinu Mulungu wanga; munditcherere khutu mau a kupemba kwanga, Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndimauza Chauta kuti, “Inu ndinu Mulungu wanga,” tcherani khutu kuti mumve liwu la kupemba kwanga, Inu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Inu Yehova, ine ndikuti, “Ndinu Mulungu wanga.” Imvani kupempha kwanga Yehova. Onani mutuwo |