Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 140:8 - Buku Lopatulika

8 Yehova, musampatse woipa zokhumba iye; musamthandize zodzipanga zake; angadzikuze.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Yehova, musampatse woipa zokhumba iye; musamthandize zodzipanga zake; angadzikuze.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Inu Chauta, musampatse munthu woipa zokhumba zake. Musathandizire chiwembu chake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Musawapatse anthu oyipa zokhumba zawo, Inu Yehova; musalole kuti zokonza zawo zitheke, mwina iwo adzayamba kunyada. Sela

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 140:8
7 Mawu Ofanana  

Ndipo wina anauza Davide nati, Ahitofele ali pakati pa opangana chiwembu pamodzi ndi Abisalomu. Davide nati, Yehova, musandulize uphungu wa Ahitofele ukhale wopusa.


Ndiye amene apatsa mafumu chipulumutso: Amene alanditsa Davide mtumiki wake kulupanga loipa.


Musandipereke ku chifuniro cha akundisautsa, chifukwa zinandiukira mboni zonama ndi iwo akupumira zachiwawa.


Ndikadapanda kuopa mkwiyo wa pa mdani, angayese molakwa outsana nao, anganene, Lakwezeka dzanja lathu, ndipo Yehova sanachite ichi chonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa