Masalimo 61:4 - Buku Lopatulika4 Ndidzagoneragonerabe m'chihema mwanu; ndidzathawira mobisalamo m'mapiko anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndidzagoneragonerabe m'chihema mwanu; ndidzathawira mobisalamo m'mapiko anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mundilole ndizikhala m'Nyumba mwanu nthaŵi zonse. Mundilole ndibisale pansi pa mapiko anu kuti munditeteze. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ine ndikulakalaka kukhala mʼtenti yanu kwamuyaya ndi kupeza chitetezo mu mthunzi wa mapiko anu. Onani mutuwo |