Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 41:4 - Buku Lopatulika

Ndinati ine, Mundichitire chifundo, Yehova; Chiritsani mtima wanga; pakuti ndachimwira Inu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndinati ine, Mundichitire chifundo, Yehova; Chiritsani mtima wanga; pakuti ndachimwira Inu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono ndidati, “Inu Chauta, ndakuchimwirani, mundikomere mtima, muchiritse moyo wanga.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndinati, “Inu Yehova, mundichitire chifundo; chiritseni pakuti ndakuchimwirani.”

Onani mutuwo



Masalimo 41:4
8 Mawu Ofanana  

Amene akhululukira mphulupulu zako zonse; nachiritsa nthenda zako zonse;


Achiritsa osweka mtima, namanga mabala ao.


Ndinavomera choipa changa kwa Inu; ndipo mphulupulu yanga sindinaibise. Ndinati, Ndidzaululira Yehova machimo anga; ndipo munakhululukira choipa cha kulakwa kwanga.


Tiyeni, tibwerere kunka kwa Yehova; pakuti wang'amba, nadzatipoletsera; wakantha, nadzatimanga.